0 Meanings
Add Yours
Follow
Share
Q&A

Mwazi Lyrics

Ukakhala iwe mphwanga
Usadzinamize uli ndi abale
Amakukonda uli ndi chuma
Ukasauka kukutaya
Amayiwala kuti mwazi ndi mwazi
Umawundana kuposa madzi

Iwe iwe mvera
Tchera tchera khutu
Ganiza ngati munthu
Song Info
Submitted by
photojaguar On Mar 16, 2010
0 Meanings

Add your song meanings, interpretations, facts, memories & more to the community.

Add your thoughts...
Questions and Answers

Ask specific questions and get answers to unlock more indepth meanings & facts.

Ask a question...